Genesis 32:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo iye anati kwa Yakobo, Dzina lako ndani? Nati iye, Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo iye anati kwa Yakobo, Dzina lako ndani? Nati iye, Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Munthuyo adamufunsa kuti, “Dzina lako ndiwe yani?” Yakobe adayankha kuti, “Dzina langa ndine Yakobe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Munthu uja anamufunsa Yakobo kuti, “Kodi dzina lako ndiwe yani?” Iye anayankha, “Ndine Yakobo.” Onani mutuwo |