Genesis 32:20 - Buku Lopatulika20 ndiponso muziti, Ndiponso, taonani, kapolo wanu Yakobo ali pambuyo pathu. Pakuti anati, Ndidzampembedzera iye ndi mphatso imene ipita patsogolo panga, pambuyo pake ndidzaona nkhope yake; kapena adzandilandira ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndiponso muziti, Ndiponso, taonani, kapolo wanu Yakobo ali pambuyo pathu. Pakuti anati, Ndidzampembedzera iye ndi mphatso imene ipita patsogolo panga, pambuyo pake ndidzaona nkhope yake; kapena adzandilandira ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Muzikati, ‘Ndiponso mtumiki wanu Yakobe ali m'mbuyo mwathumu.’ ” Yakobe ankaganiza kuti, “Ndimtsitsa mtima ndi mphatso zimene ndamtumizirazi, ndipo ndikakumana naye, mwina adzandilandira bwino.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Muzikanena kuti, ‘Wantchito wanu Yakobo akubwera mʼmbuyo mwathumu.’ ” Popeza anaganiza kuti, “Ndidzamutsitsa mtima ndi mphatso ndazitsogozazi. Apo tsono ndikadzakumana naye, mwina adzandilandira bwino.” Onani mutuwo |