Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 32:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Yakobo anankabe ulendo wake, ndipo amithenga a Mulungu anakomana naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yakobo anankabe ulendo wake, ndipo amithenga a Mulungu anakomana naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Yakobe adanyamuka ulendo wake, ndipo angelo a Mulungu adakumana naye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Nayenso Yakobo analowera njira yake, ndipo angelo a Mulungu anakumana naye.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 32:1
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anapita atatha kunena naye Abrahamu: ndipo Abrahamu anabwera kumalo kwake.


Ndipo anamdalitsa Rebeka, nati kwa iye, Mlongo wathu ndiwe, iwe ukhale amai wa anthu zikwizikwi, mbeu zako zigonjetse chipata cha iwo akudana nao.


Ndipo sunandiloleze ine ndimpsompsone ana anga aamuna ndi aakazi? Wapusa iwe pakuchita chotero.


Mngelo wa Yehova azinga kuwatchinjiriza iwo akuopa Iye, nawalanditsa iwo.


Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe, akusunge m'njira zako zonse.


ngati Paulo, kapena Apolo, kapena Kefa, kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena za makono ano, kapena zilinkudza; zonse ndi zanu;


kuti mu Mpingo azindikiritse tsopano kwa akulu ndi maulamuliro m'zakumwamba nzeru ya mitundumitundu ya Mulungu,


atakhala wakuposa angelo, monga momwe adalowa dzina lakuposa iwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa