Genesis 31:9 - Buku Lopatulika9 Chomwecho Mulungu anazichotsa zoweta za atate wanu, nandipatsa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Chomwecho Mulungu anazichotsa zoweta za atate wanu, nandipatsa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mulungu watenga zoŵeta zonse kwa bambo wanu, wapatsa ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Motero Mulungu walanda abambo anu ziweto zawo ndi kundipatsa. Onani mutuwo |