Genesis 31:54 - Buku Lopatulika54 Ndipo Yakobo anapereka nsembe paphiripo, naitana abale ake kuti adye chakudya; ndipo anadya chakudya, nagona paphiripo usiku wonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 Ndipo Yakobo anapereka nsembe paphiripo, naitana abale ake kuti adye chakudya; ndipo anadya chakudya, nagona paphiripo usiku wonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Tsono Yakobe adapereka nsembe paphiripo, naitana anthu ake kuti adzadye chakudya. Atamaliza kudyako, adagona paphiri pomwepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 Yakobo anapereka nsembe pa phiri paja, ndipo anayitana abale ake kuti adzadye chakudya. Atadya chakudya anagona pa phiri pomwepo. Onani mutuwo |