Genesis 31:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo iye anatenga abale ake pamodzi naye, namlondola iye ulendo wa masiku asanu ndi awiri: nampeza iye paphiri la Giliyadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo iye anatenga abale ake pamodzi naye, namlondola iye ulendo wa masiku asanu ndi awiri: nampeza iye paphiri la Giliyadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Tsono adatenga anthu ake, nkulondola Yakobeyo masiku asanu ndi aŵiri, mpaka adakampezera ku dziko lamapiri la Giliyadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Pomwepo anatengana ndi abale ake namulondola Yakobo kwa masiku asanu ndi awiri ndipo anakamupezera ku Giliyadi, dziko la mapiri. Onani mutuwo |