Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 31:22 - Buku Lopatulika

22 Tsiku lachitatu anamuuza Labani kuti Yakobo wathawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Tsiku lachitatu anamuuza Labani kuti Yakobo wathawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Patapita masiku atatu, Labani adamva kuti Yakobe adathaŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Patapita masiku atatu, Labani anawuzidwa kuti Yakobo wathawa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 31:22
5 Mawu Ofanana  

Ndipo iye yekha anatalikitsana ndi Yakobo ulendo wa masiku atatu: ndipo Yakobo anadyetsa ziweto zina za Labani.


Ndipo anathawa iye ndi zonse anali nazo: ndipo anauka naoloka panyanja naloza nkhope yake iyang'anire kuphiri la Giliyadi.


Ndipo iye anatenga abale ake pamodzi naye, namlondola iye ulendo wa masiku asanu ndi awiri: nampeza iye paphiri la Giliyadi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa