Genesis 31:11 - Buku Lopatulika11 Mthenga wa Mulungu ndipo anati kwa ine m'kulotamo, Yakobo; nati ine, Ndine pano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mthenga wa Mulungu ndipo anati kwa ine m'kulotamo, Yakobo; nati ine, Ndine pano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo mngelo wa Mulungu adalankhula nane m'maloto momwemo nandiitana kuti, ‘Yakobe,’ ine ndidayankha kuti, ‘Ee Ambuye!’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kutulo komweko, mngelo wa Mulungu anati, ‘Yakobo.’ Ine ndinayankha, ‘Ee, Ambuye.’ Onani mutuwo |