Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 30:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo iye anati kwa Labani, Udziwa iwe chomwe ndakutumikira iwe ndi chomwe zachita zoweta zako ndi ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo iye anati kwa Labani, Udziwa iwe chomwe ndakutumikira iwe ndi chomwe zachita zoweta zako ndi ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Yakobe adayankha kuti, “Mukudziŵa m'mene ndakugwirirani ntchito, ndi m'mene zoŵeta zanu zaswanirana kwambiri pozisamala ine.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Koma Yakobo anati kwa iye, “Inu mukudziwa mmene ine ndakugwirirani ntchito ndi mmene ziweto zanu zaswanira pamene ine ndimazisamalira.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 30:29
10 Mawu Ofanana  

Chifukwa ndisadafike ine, iwe unali nazo zowerengeka, ndipo zachuluka zambirimbiri; Yehova wakudalitsa iwe kulikonse ndinayendako: tsopano ndidzamanga liti banja langa?


Ndipo Biliha anatenga pakati, nambalira Yakobo mwana wamwamuna.


Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.


Ndani kodi ali kapolo wokhulupirika ndi wanzeru, amene mbuye wake anamkhazika woyang'anira banja lake, kuwapatsa zakudya pa nthawi yake?


Pakuti chifuniro cha Mulungu chitere, kuti ndi kuchita zabwino mukatontholetse chipulukiro cha anthu opusa;


Anyamata inu, gonjerani ambuye anu ndi kuopa konse, osati abwino ndi aulere okha, komanso aukali.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa