Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 30:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo iye anati, Undipangire ine malipiro ako, ndipo ndidzakupatsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo iye anati, Undipangire ine malipiro ako, ndipo ndidzakupatsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Tandiwuza malipiro ako, ndikupatsa.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Anapitiriza kunena kuti, “Tchula malipiro ako ndipo ndidzakupatsa.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 30:28
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Labani anati kwa Yakobo, Chifukwa iwe ndiwe mbale wanga, kodi udzanditumikira ine kwachabe? Undiuze ine, malipiro ako adzakhala otani?


Ndipo anati Labani, Kuli kwabwino kuti ndimpatse iwe osampatsa kwa mwamuna wina; ukhalebe ndi ine.


Ndinakhala chotere zaka makumi awiri m'nyumba mwako; zaka khumi ndi zinai ndinakutumikira iwe chifukwa cha ana ako aakazi awiri, ndi zaka zisanu ndi chimodzi chifukwa cha zoweta zako; wasintha malipiro anga kakhumi.


Ndipo atate wanu wandinyenga ine, nasinthanitsa malipiro anga kakhumi; koma Mulungu sanamlole iye andichitire ine choipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa