Genesis 29:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yakobo ananka ulendo wake, nafika ku dziko la anthu a kum'mawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yakobo ananka ulendo wake, nafika ku dziko la anthu a kum'mawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono Yakobe adapitirira ulendo wake, kupita ku dziko la anthu akuvuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yakobo anapitiriza ulendo wake kupita ku dziko la anthu a kummawa. Onani mutuwo |