Genesis 28:7 - Buku Lopatulika7 ndiponso kuti Yakobo anamvera atate wake ndi amake, nanka ku Padanaramu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ndiponso kuti Yakobo anamvera atate wake ndi amake, nanka ku Padanaramu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adamva kuti Yakobe wamvera bambo wake ndi mai wake, ndipo kuti wapita ku Mesopotamiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yakobo anamvera abambo ake ndi amayi ake ndi kupita ku Padanaramu. Onani mutuwo |