Genesis 28:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Isaki anamlola Yakobo amuke, ndipo ananka ku Padanaramu kwa Labani, mwana wake wa Betuele Mwaramu, mlongo wake wa Rebeka, amai wao wa Yakobo ndi Esau. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Isaki anamlola Yakobo amuke, ndipo ananka ku Padanaramu kwa Labani, mwana wake wa Betuele Mwaramu, mlongo wake wa Rebeka, amai wao wa Yakobo ndi Esau. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Atatero Isaki adatumiza Yakobe ku Mesopotamiya kwa Labani, mwana wa Betuele Mwaramu. Labani anali mlongo wa Rebeka mai wa Yakobe ndi Esau. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo Isake anamulola Yakobo kuti anyamuke kupita ku Padanaramu kwa Labani mwana wa Betueli Mwaramu. Labani anali mlongo wa Rebeka, mayi wa Yakobo ndi Esau. Onani mutuwo |