Genesis 27:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo Isaki atate wake anayankha nati kwa iye, Taona, pokhala pako mpa zonenepa za dziko lapansi, pa mame a kumwamba akudzera komwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo Isaki atate wake anayankha nati kwa iye, Taona, pokhala pako mpa zonenepa za dziko lapansi, pa mame a kumwamba akudzera komwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Tsono Isaki, bambo wakeyo, adamuuza kuti, “Pa malo ako okhalapo sipadzakhala konse chonde, mvula siidzagwa pa minda yako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Tsono Isake abambo ake anamuyankha kuti, “Malo ako okhalapo sadzabala dzinthu, ndipo mvula sidzagwa pa minda yako. Onani mutuwo |