Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo panali atatha Isaki kumdalitsa Yakobo, atatuluka Yakobo pamaso pa Isaki atate wake, Esau mkulu wake analowa kuchokera kuthengo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo panali atatha Isaki kumdalitsa Yakobo, atatuluka Yakobo pamaso pa Isaki atate wake, Esau mkulu wake analowa kuchokera kuthengo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Isaki atamaliza kudalitsako, Yakobe adachokapo. Nthaŵi yomweyo wafika Esau kuchokera kuuzimba kuja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Isake atatsiriza kudalitsa Yakobo, atangochoka pamaso pa abambo akewo, Esau anabwera kuchokera kosaka kuja.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:30
4 Mawu Ofanana  

Iye ndiye mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova: chifukwa chake kunanenedwa, Monga Nimirodi mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova.


Anthu akutumikire iwe, mitundu ikuweramire iwe; uchite ufumu pa abale ako, ana a amai ako akuweramire iwe. Wotemberereka aliyense akutemberera iwe, wodalitsika aliyense akudalitsa iwe.


Ndipo iyenso anakonza chakudya chokolera, nadza nacho kwa atate wake, nati kwa atate wake, Auke atate wanga, adye nyama ya mwana wake, kuti moyo wanu undidalitse ine.


Pakuti mudziwa kutinso pamene anafuna kulowa dalitsolo, anakanidwa (pakuti sanapeze malo akulapa), angakhale analifunafuna ndi misozi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa