Genesis 26:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo analawira m'mamawa nalumbirirana wina ndi mnzake; ndipo Isaki anawalola amuke, ndipo anauka kuchokera kwa iye m'mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo analawira m'mamawa nalumbirirana wina ndi mnzake; ndipo Isaki anawalola amuke, ndipo anauka kuchokera kwa iye m'mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 M'maŵa kutacha, munthu aliyense adalonjeza ndi kulumbira. Kenaka Isaki adaŵaperekeza, ndipo onsewo adachoka mwamtendere, napita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Mmawa wake aliyense analumbira pangano kwa mnzake. Tsono Isake anawalola kuti anyamuke ndipo anamusiya mu mtendere. Onani mutuwo |