Genesis 25:4 - Buku Lopatulika4 Ana a Midiyani: Efa, ndi Efere, ndi Hanoki, ndi Abida, ndi Elida. Onse amenewa ndi ana a Ketura. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ana a Midiyani: Efa, ndi Efere, ndi Hanoki, ndi Abida, ndi Elida. Onse amenewa ndi ana a Ketura. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ana a Midiyani anali Efa, Efera, Hanoki, Abida ndi Elida. Onseŵa anali zidzukulu za Ketura. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura. Onani mutuwo |