Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:62 - Buku Lopatulika

62 Ndipo Isaki anadzera njira ya Beere-Lahai-Roi; chifukwa kuti anakhala iye m'dziko la kumwera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

62 Ndipo Isaki anadzera njira ya Beere-Lahai-Roi; chifukwa kuti anakhala iye m'dziko la kumwera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

62 Isaki anali atachoka kuchipululu kumene kunali chitsime cha Wamoyo-Wondipenya chija, kukakhala m'chigawo chakumwera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

62 Pa nthawiyi nʼkuti Isake atafika kuchokera ku chitsime cha Wamoyo Wondipenya (Beeri-lahai-roi), popeza tsopano ankakhala ku Negevi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:62
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anayenda ulendo wake, nayendayenda kunka kumwera.


Chifukwa chake chitsimecho chinatchedwa Beere-Lahai-Roi; taonani chili pakati pa Kadesi ndi Beredi.


Abrahamu ndipo anachoka kumeneko kunka ku dziko la kumwera, ndipo anakhala pakati pa Kadesi ndi Suri, ndipo anakhala ngati mlendo mu Gerari.


Ndipo adauka Rebeka ndi anamwali ake, nakwera pa ngamira natsata munthuyo: mnyamatayo ndipo anamtenga Rebeka namuka.


Ndipo panali atafa Abrahamu, Mulungu anamdalitsa Isaki mwana wake; ndipo Isaki anakhala pa Beere-Lahai-Roi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa