Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 24:57 - Buku Lopatulika

57 Ndipo anati iwo, Tidzamuitana namwaliyo, tidzamfunsa pakamwa pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 Ndipo anati iwo, Tidzamuitana namwaliyo, tidzamfunsa pakamwa pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Apo iwowo adayankha kuti, “Tiyeni timuitane namwaliyo, kuti timve zimene iyeyo anene.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 Koma iwo anati, “Bwanji timuyitane mtsikanayo ndipo timufunse ngati afuna kupita nanu panopa.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 24:57
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati kwa iwo, Musandichedwetse ine, pakuti Yehova wandiyendetsa bwino m'njira yanga: mundilole ine ndinke kwa mbuyanga.


Ndipo anamuitana Rebeka nati kwa iye, Kodi udzanka pamodzi ndi munthuyo? Ndipo anati, Ndidzanka.


Cholamulira Yehova za ana aakazi a Zelofehadi ndi ichi, kuti, Akwatibwe nao amene afuna eni ake; komatu akwatibwe nao a banja la fuko la makolo ao okhaokha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa