Genesis 24:50 - Buku Lopatulika50 Ndipo anayankha Labani ndi Betuele, nati, Chatuluka kwa Yehova chinthu ichi; sitingathe kunena ndi iwe choipa kapena chabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Ndipo anayankha Labani ndi Betuele, nati, Chatuluka kwa Yehova chinthu ichi; sitingathe kunena ndi iwe choipa kapena chabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Pamenepo Labani ndi Betuele adauza munthuyo kuti, “Popeza kuti zimenezi nzochokera kwa Chauta, ife sitingachitepo kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Labani ndi Betueli anayankha nati, “Izi ndi zochokera kwa Yehova, ndipo ife sitinganenepo kanthu. Onani mutuwo |