Genesis 24:21 - Buku Lopatulika21 Munthuyo ndipo anamyang'anira iye, nakhala chete, kuti adziwe ngati Yehova anamuyendetsa bwino kapena iai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Munthuyo ndipo anamyang'anira iye, nakhala chete, kuti adziwe ngati Yehova anamuyendetsa bwino kapena iai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Munthu uja anali phee, kuyang'ana zimene ankachita namwaliyo, kuti aone ngati Chauta wadalitsa ulendo wake kapena ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Modekha, munthu uja anayangʼanitsitsa kwambiri mtsikana uja kuti adziwedi ngati Yehova anamutsogolera pa ulendo wake uja kapena ayi. Onani mutuwo |