Genesis 24:13 - Buku Lopatulika13 Taonani, ine ndiima pa chitsime cha madzi; ndipo ana aakazi a m'mzinda atuluka kudzatunga madzi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Taonani, ine ndiima pa chitsime cha madzi; ndipo ana akazi a m'mudzi atuluka kudzatunga madzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndili pano pa chitsime, ndipo akazi amumzindamu abwera kudzatunga madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Taonani ndayima pambali pa chitsimechi, ndipo atsikana a mu mzindawu akubwera kudzatunga madzi. Onani mutuwo |