Genesis 24:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Abrahamu anali wokalamba, nagonera zaka zambiri; ndipo Yehova anadalitsa Abrahamu m'zinthu zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Abrahamu anali wokalamba, nagonera zaka zambiri; ndipo Yehova anadalitsa Abrahamu m'zinthu zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsopano Abrahamu anali atakalamba, atagonera zaka zochuluka, ndipo Mulungu adaamudalitsa pa zonse zimene ankachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsopano Abrahamu anali atakalamba kwambiri, ndipo Yehova anamudalitsa mu zonse anachita. Onani mutuwo |