Genesis 23:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo ana a Hiti analimbitsira Abrahamu munda, ndi phanga lili m'menemo, likhale lake lamanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo ana a Hiti analimbitsira Abrahamu munda, ndi phanga lili m'menemo, likhale lake lamanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Motero mundawo pamodzi ndi manda omwewo amene kale adaali a Ahiti, malo onsewo adapatsidwa kwa Abrahamu, ndipo iye adaŵasandutsa manda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Choncho Ahiti anapereka munda pamodzi ndi phanga la mʼmenemo kwa Abrahamu kuti akhale manda. Onani mutuwo |