Genesis 23:18 - Buku Lopatulika18 inalimbitsidwa kwa Abrahamu ikhale yake, pamaso pa ana a Hiti, pa onse amene analowa pa chipata cha mzinda wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 inalimbitsidwa kwa Abrahamu ikhale yake, pamaso pa ana a Hiti, pa onse amene analowa pa chipata cha mudzi wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ahiti amene anali pamsonkhanopo adachitira umboni kuti dera lonselo ndi la Abrahamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 kwa Abrahamu ngati chuma chake pamaso pa anthu onse a ku Hiti amene anabwera ku chipata cha mzindawo. Onani mutuwo |