Genesis 22:21 - Buku Lopatulika21 Uzi woyamba ndi Buzi mphwake, ndi Kemuwele atate wake wa Aramu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Uzi woyamba ndi Buzi mphwake, ndi Kemuwele atate wake wa Aramu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mwana wake wachisamba anali Uzi, mng'ono wa Uziyo anali Buzi. Panalinso Kemuwele, bambo wake wa Aramu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Woyamba anali Huzi ndipo kenaka mʼbale wake Buzi. Anaberekanso Kemueli, amene anali abambo ake a Aramu. Onani mutuwo |