Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 22:21 - Buku Lopatulika

21 Uzi woyamba ndi Buzi mphwake, ndi Kemuwele atate wake wa Aramu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Uzi woyamba ndi Buzi mphwake, ndi Kemuwele atate wake wa Aramu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Mwana wake wachisamba anali Uzi, mng'ono wa Uziyo anali Buzi. Panalinso Kemuwele, bambo wake wa Aramu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Woyamba anali Huzi ndipo kenaka mʼbale wake Buzi. Anaberekanso Kemueli, amene anali abambo ake a Aramu.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 22:21
9 Mawu Ofanana  

Ndipo panali zitapita izi, anauza Abrahamu kuti, Taonani, Milika iyenso anambalira Nahori mphwako ana;


ndi Kesedi, ndi Hazo, ndi Pilidasi ndi Yidilafi, ndi Betuele.


Ndipo mnyamatayo anatenga ngamira khumi za mbuyake, namuka: chifukwa kuti chuma chonse cha mbuyake chinali m'dzanja lake: ndipo anachoka namuka ku Mesopotamiya, kumzinda wa Nahori.


Panali munthu m'dziko la Uzi, dzina lake ndiye Yobu; ndipo munthuyu anali wangwiro ndi woongoka, wakuopa Mulungu ndi kupewa zoipa.


Ndipo adapsa mtima Elihu mwana wa Barakele wa ku Buzi, wa chibale cha Ramu, adapsa mtima pa Yobu; pakuti anadziyesera yekha wolungama, wosati Mulungu.


ndi anthu onse osakanizidwa, ndi mafumu onse a dziko la Uzi, ndi mafumu onse a dziko la Afilisti, ndi Asikeloni, ndi Gaza, ndi Ekeroni, ndi otsala a Asidodi,


Dedani, ndi Tema, ndi Buzi, ndi onse amene ameta m'mbali mwa tsitsi;


Ndipo ananena fanizo lake, nati, Ku Aramu ananditenga Balaki, mfumu ya Mowabu ananditenga ku mapiri a kum'mawa, Idza, udzanditembererere Yakobo. Idza, nudzanyoze Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa