Genesis 22:18 - Buku Lopatulika18 m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsidwa: chifukwa wamvera mau anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsidwa: chifukwa wamvera mau anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndipo mitundu yonse ya pa dziko lapansi idzalandira madalitso kudzera mwa zidzukulu zako, chifukwa iwe wandimvera.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 ndipo kudzera mwa chidzukulu chako, mitundu yonse ya anthu pa dziko lapansi idzadalitsika, chifukwa iwe wandimvera.” Onani mutuwo |