Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 22:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Abrahamu anatambasula dzanja lake, natenga mpeni kuti amuphe mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Abrahamu anatambasula dzanja lake, natenga mpeni kuti amuphe mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono adasolola mpeni kuti amuphe mwana wakeyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kenaka Abrahamu anatambasula dzanja lake natenga mpeni kuti aphe mwana wake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 22:10
6 Mawu Ofanana  

Koma mthenga wa Yehova anamuitana iye ndi mau odzera kumwamba, nati, Abrahamu, Abrahamu; ndi iye anati, Ndine pano.


m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsidwa: chifukwa wamvera mau anga.


Ndipo anafika kumalo komwe Mulungu anamuuza iye; ndipo Abrahamu anamanga guwa la nsembe nakonza nkhuni, namanga Isaki mwana wake, namuika iye paguwa la nsembe pamwamba pa nkhuni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa