Genesis 21:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Sara anaona mwana wake wamwamuna wa Hagara Mwejipito, amene anambalira Abrahamu, alinkuseka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Sara anaona mwana wake wamwamuna wa Hagara Mwejipito, amene anambalira Abrahamu, alinkuseka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsiku lina Ismaele, amene Hagara Mwejipito uja adabalira Abrahamu, ankamunyoza Isaki mwana wa Sara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma Sara anaona kuti mwana wamwamuna amene Hagara Mwigupto anamuberekera Abrahamu amamuseka, Onani mutuwo |