Genesis 21:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anakula mwanayo naletsedwa kuyamwa: ndipo Abrahamu anakonza madyerero aakulu tsiku lomwe analetsedwa Isaki kuyamwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anakula mwanayo naletsedwa kuyamwa: ndipo Abrahamu anakonza madyerero akulu tsiku lomwe analetsedwa Isaki kuyamwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mwanayo adakula, ndipo pa tsiku lakuti amuletsa kuyamwa, Abrahamu adachita phwando lalikulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mwana uja anakula mpaka kumuletsa kuyamwa. Tsiku lomuletsa Isake kuyamwa, Abrahamu anakonza phwando lalikulu. Onani mutuwo |