Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 21:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo Abrahamu anamdzudzula Abimeleki chifukwa cha chitsime cha madzi, anyamata ake a Abimeleki anachilanda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo Abrahamu anamdzudzula Abimeleki chifukwa cha chitsime cha madzi, anyamata ake a Abimeleki anachilanda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Pambuyo pake Abrahamu adamdandaulira Abimeleki za chitsime chimene antchito ake adaalanda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Kenaka Abrahamu anadandaula kwa Abimeleki pa za chitsime chimene antchito a Abimeleki analanda.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 21:25
11 Mawu Ofanana  

Ndipo panali ndeu, abusa a Abramu kudana ndi abusa a Loti. Akanani ndi Aperizi ndipo analinkukhala nthawi yomweyo m'dzikomo.


Ndipo Abrahamu anati, Ine ndidzalumbira.


Ndipo anati Abimeleki, Sindinadziwe amene anachita icho; ndipo iwe sunandiuze ine, ndiponso sindinamve koma lero lino.


Ndipo anati, Sitingathe, koma zitasonkhana ziweto zonse, ndipo atagubuduza mwala kuuchotsa pakamwa pa chitsime ndiko; pamenepo ndipo tizimwetsa nkhosa.


Chidzudzulo chilowa m'kati mwa wozindikira, kopambana ndi kukwapula wopusa kwambiri.


Nena mlandu wako ndi mnzako, osawulula zinsinsi za mwini;


Chidzudzulo chomveka chiposa chikondi chobisika.


Ndipo ngati mbale wako akuchimwira iwe, pita, numlangize pa nokha iwe ndi iye; ngati akumvera iwe, wambweza mbale wako.


Ndipo anati kwa iye, Mundipatse dalitso; popeza mwandipatsa dziko la kumwera, ndipatsenso zitsime za madzi. Pamenepo Kalebe anampatsa zitsime za kumtunda ndi zitsime za kunsi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa