Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 21:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo anati Abimeleki, Sindinadziwe amene anachita icho; ndipo iwe sunandiuze ine, ndiponso sindinamve koma lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo anati Abimeleki, Sindinadziwe amene anachita icho; ndipo iwe sunandiuze ine, ndiponso sindinamve koma lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Abimeleki adati, “Sindikudziŵa amene adachita zimenezi. Ngakhale inu nomwe simudandiwuze, ndipo ine kumva nkomweku.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Koma Abimeleki anati, “Ine sindikudziwa amene anachita zimenezi. Iwe sunandiwuze, ndipo ndazimva lero zimenezi.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 21:26
4 Mawu Ofanana  

Ndipo panali ndeu, abusa a Abramu kudana ndi abusa a Loti. Akanani ndi Aperizi ndipo analinkukhala nthawi yomweyo m'dzikomo.


Ndipo Abrahamu anamdzudzula Abimeleki chifukwa cha chitsime cha madzi, anyamata ake a Abimeleki anachilanda.


Ndipo Abrahamu anatenga nkhosa ndi ng'ombe, nampatsa Abimeleki, ndipo anapangana pangano onse awiriwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa