Genesis 21:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo anakhala m'chipululu cha Parani; ndipo amake anamtengera iye mkazi wa ku dziko la Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo anakhala m'chipululu cha Parani; ndipo amake anamtengera iye mkazi wa ku dziko la Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mai wakeyo adampezera mkazi wa ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Akukhala ku chipululu cha Parani, mayi ake anamupezera mkazi wochokera ku Igupto. Onani mutuwo |