Genesis 21:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo Mulungu anakhala ndi mnyamata, ndipo anakula iye; nakhala m'chipululu, nakhala wauta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo Mulungu anakhala ndi mnyamata, ndipo anakula iye; nakhala m'chipululu, nakhala wauta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Mulungu adakhala naye mwanayo mpaka kukula. Adakulira m'chipululu cha Perani, nasanduka katswiri wa uta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mulungu anali ndi mnyamatayo pamene ankakula. Anakhala ku chipululu nakhala katswiri wolasa uta. Onani mutuwo |