Genesis 21:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anatha madzi a m'thumba ndipo anaika mwana pansi pa chitsamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anatha madzi a m'mchenje ndipo anaika mwana pansi pa chitsamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono madzi aja atamthera, adangosiya mwanayo pa chitsamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Madzi atatha mʼbotolo muja, anamuyika mnyamatayo pansi pa zitsamba. Onani mutuwo |