Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 21:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo mauwo anaipira Abrahamu chifukwa cha mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo mauwo anaipira Abrahamu chifukwa cha mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Zimenezi zidamuvuta kwambiri Abrahamu, chifukwa chakuti Ismaele nayenso anali mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Nkhaniyi inamumvetsa chisoni kwambiri Abrahamu chifukwa imakhudza mwana wake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 21:11
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anati kwa Mulungu, Ha! Ismaele akhale ndi moyo pamaso panu!


Ndipo Mulungu anati kwa Abrahamu, Usaipidwe nao, chifukwa cha mnyamatayo, ndi chifukwa cha mdzakazi wako; momwe monse akunenera iwe Sara umvere iwe mau ake; chifukwa kuti mwa Isaki zidzaitanidwa mbeu zako.


Ndipo mfumuyo inagwidwa chisoni, nikwera ku chipinda chosanja pa chipatacho, nilira misozi; niyenda, nitero, Mwana wanga Abisalomu, mwana wanga Abisalomu; mwana wanga! Mwenzi nditakufera ine, Abisalomu, mwana wanga, mwana wanga!


Iye wakukonda atate wake, kapena amake koposa Ine, sayenera Ine, ndipo iye wakukonda mwana wake wamwamuna, kapena wamkazi koposa Ine, sayenera Ine.


Chilango chilichonse, pakuchitika, sichimveka chokondweretsa, komatu chowawa; koma chitatha, chipereka chipatso cha mtendere, kwa iwo ozoloweretsedwa nacho, ndicho cha chilungamo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa