Genesis 21:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo mauwo anaipira Abrahamu chifukwa cha mwana wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo mauwo anaipira Abrahamu chifukwa cha mwana wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Zimenezi zidamuvuta kwambiri Abrahamu, chifukwa chakuti Ismaele nayenso anali mwana wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Nkhaniyi inamumvetsa chisoni kwambiri Abrahamu chifukwa imakhudza mwana wake. Onani mutuwo |