Genesis 2:24 - Buku Lopatulika24 Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Nʼchifukwa chake, mwamuna amasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake ndipo awiriwo amakhala thupi limodzi. Onani mutuwo |