Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 2:20 - Buku Lopatulika

20 Adamu ndipo anazitcha maina zinyama zonse, ndi mbalame za m'mlengalenga ndi zamoyo zonse za m'thengo: koma kwa Adamu sanapezeke womthangatira iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Adamu ndipo anazitcha maina zinyama zonse, ndi mbalame za m'mlengalenga ndi zamoyo zonse za m'thengo: koma kwa Adamu sanapezedwa womthangatira iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Adamu adazitcha maina nyama zonse, mbalame ndi zamoyo zonse zakuthengo. Komabe panalibe mnzake woti azimthandiza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Choncho Adamu anazitcha mayina ziweto zonse, mbalame zamlengalenga ndi nyama zakuthengo zonse. Komabe munthu uja analibe mnzake womuthandiza.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 2:20
3 Mawu Ofanana  

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.


Koma Yehova Mulungu anamgonetsa Adamu tulo tatikulu, ndipo anagona; ndipo anatengako nthiti yake imodzi, natsekapo ndi mnofu pamalo pake.


nkhosa ndi ng'ombe, zonsezo, ndi nyama zakuthengo zomwe;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa