Genesis 2:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Yehova Mulungu anatenga munthuyo, namuika iye m'munda wa Edeni kuti aulime nauyang'anire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Yehova Mulungu anatenga munthuyo, namuika iye m'munda wa Edeni kuti aulime nauyang'anire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono Chauta adamtenga munthuyo, namukhazika m'munda wa Edeni uja kuti azilima ndi kumausamala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Yehova Mulungu anatenga munthu uja ndi kumuyika mʼmunda wa Edeni kuti awulime ndi kuwusamalira. Onani mutuwo |