Genesis 19:10 - Buku Lopatulika10 Koma anthu aja anatulutsa dzanja lao, namlowetsa Loti momwe anali iwo m'nyumba, natseka pakhomo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Koma anthu aja anatulutsa dzanja lao, namlowetsa Loti momwe anali iwo m'nyumba, natseka pakhomo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma anthu aŵiri anali m'kati aja adamkokera Lotiyo m'nyumba, natseka chitseko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Koma anthu aja anali mʼkatiwa anasuzumira namukokera Loti uja mʼkati mwa nyumba nʼkutseka chitseko. Onani mutuwo |