Genesis 17:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo analeka kunena naye, ndipo Mulungu anakwera kuchokera kwa Abrahamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo analeka kunena naye, ndipo Mulungu anakwera kuchokera kwa Abrahamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mulungu atatha kulankhula ndi Abrahamu, adamsiya pomwepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Atatha kuyankhula, Mulungu anamuchokera Abrahamu. Onani mutuwo |