Genesis 17:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo mwamuna wosadulidwa, wosadulidwa khungu lake, munthuyo amsadze mwa anthu a mtundu wake; waphwanya pangano langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo mwamuna wosadulidwa, wosadulidwa khungu lake, munthuyo amsadze mwa anthu a mtundu wake; waphwanya pangano langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Munthu wamwamuna wosaumbalidwa adzachotsedwa pakati pa anthu a mtundu wake, chifukwa sadasunge chipangano changa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Mwamuna aliyense amene adzakhala wosachita mdulidwe adzachotsedwa pakati pa anthu ake chifukwa sanasunge pangano langa.” Onani mutuwo |