Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 15:11 - Buku Lopatulika

11 Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Miphamba idadzatera kuti idye nyama zimene adaaphazo, koma Abramu adaipirikitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Pamene miphamba inabwera kuti itole nyama ija, Abramu anayipirikitsa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 15:11
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenga iye zonse zimenezo, nazidula pakati, naika bandu popenyana ndi linzake: koma mbalame sanazidule.


Ndipo linalinkulowa dzuwa, ndi tulo tatikulu tinamgwera Abramu: ndipo taonani, kuopsa kwa mdima waukulu kunamgwera iye.


Ndinafotokozera ndi milomo yanga maweruzo onse a pakamwa panu.


nuziti, Atero Ambuye Yehova, Chiombankhanga chachikulu ndi mapiko aakulu, ndi maphiphi aatali, odzala nthenga cha mathothomathotho, chinafika ku Lebanoni, nkutenga nsonga ya mkungudza,


Panalinso chiombankhanga china chachikulu, ndi mapiko aakulu, ndi nthenga zambiri; ndipo taona, mpesa uwu unachipindira mizu yake, nuchilunjikitsira zake, kuchokera pookedwa pake, kuti chiuthirire madzi.


Ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndipo zinadza mbalame, nkulusira izo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa