Genesis 15:11 - Buku Lopatulika11 Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pamene miimba inatsikira panyama, Abramu anaingitsa iyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Miphamba idadzatera kuti idye nyama zimene adaaphazo, koma Abramu adaipirikitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pamene miphamba inabwera kuti itole nyama ija, Abramu anayipirikitsa. Onani mutuwo |