Genesis 14:3 - Buku Lopatulika3 Onse amenewo anadziphatikana pa chigwa cha Sidimu (pamenepo ndi pa Nyanja ya Mchere). Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Onse amenewo anadziphatikana pa chigwa cha Sidimu (pamenepo ndi pa Nyanja ya Mchere). Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mafumu asanu ameneŵa adasonkhana pamodzi ndi ankhondo ao onse m'chigwa cha Sidimu, (ku Nyanja Yakufa). Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mafumu onse anathiridwa nkhondowa anagwirizana pamodzi kupita ku Chigwa cha Sidimu (Nyanja ya Mchere). Onani mutuwo |