Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 10:30 - Buku Lopatulika

30 Kwao kunayamba pa Mesa pakunka ku Sefari phiri la kum'mawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Kwao kunayamba pa Mesa pakunka ku Sefari phiri la kum'mawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Dziko limene ankakhalamo lidayambira ku Mesa kumaloŵa ku Sefari ku mapiri chakuvuma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Chigawo chimene ankakhala chinayambira ku Mesa mpaka ku Seferi, ku dera la mapiri chakummawa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 10:30
3 Mawu Ofanana  

ndi Ofiri ndi Havila, ndi Yobabu; onse amenewa ndi ana a Yokotani.


Amenewa ndi ana a Semu, monga mwa mabanja ao, mwa zinenedwe zao, m'maiko ao, m'mitundu yao.


Ndipo ananena fanizo lake, nati, Ku Aramu ananditenga Balaki, mfumu ya Mowabu ananditenga ku mapiri a kum'mawa, Idza, udzanditembererere Yakobo. Idza, nudzanyoze Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa