Genesis 1:17 - Buku Lopatulika17 Mulungu ndipo adaika zimenezo m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire padziko lapansi, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Mulungu ndipo adaika zimenezo m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mulungu adaika miyuniyo ku thambo, kuti iziwunikira dziko lapansi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mulungu anaziyika mlengalenga kuti ziziwunikira pa dziko lapansi, Onani mutuwo |