Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 9:35 - Buku Lopatulika

35 Potero mtima wa Farao unalimba, ndipo sanalole ana a Israele amuke; monga Yehova adalankhula mwa Mose.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Potero mtima wa Farao unalimba, ndipo sanalole ana a Israele amuke; monga Yehova adalankhula mwa Mose.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Adakhala wokanika kwambiri, ndipo sadalole kuti Aisraele apite monga momwe Chauta adaauzira Mose muja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Choncho Farao sanalole kuti Aisraeli apite monga momwe Yehova anamuwuzira Mose.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 9:35
4 Mawu Ofanana  

Koma Ine ndidziwa kuti mfumu ya Aejipito siidzalola inu kumuka, inde lingakhale ndi dzanja lamphamvu ai.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Pakumuka iwe kubwerera kunka ku Ejipito, usamalire uchite zozizwa zonse ndaziika m'dzanja lako, pamaso pa Farao; koma Ine ndidzalimbitsa mtima wake kuti asadzalole anthu kupita.


Koma mtima wa Farao unalimba, ndipo sanamvere iwo; monga adalankhula Yehova.


Pamene Farao anaona kuti mvula ndi matalala ndi mabingu zidaleka anaonjezanso kuchimwa, naumitsa mtima wake, iye ndi anyamata ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa