Eksodo 9:32 - Buku Lopatulika32 Koma tirigu ndi rai sizinayoyoke popeza amabzala m'mbuyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Koma tirigu ndi rai sizinayoyoka popeza amabzala m'mbuyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Koma tirigu ndi rayi sizidaonongeke, chifukwa zimenezi amabzala mochedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Koma tirigu ndi mchewere sizinawonongeke chifukwa zimakhwima mochedwa. Onani mutuwo |