Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 9:32 - Buku Lopatulika

32 Koma tirigu ndi rai sizinayoyoke popeza amabzala m'mbuyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Koma tirigu ndi rai sizinayoyoka popeza amabzala m'mbuyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Koma tirigu ndi rayi sizidaonongeke, chifukwa zimenezi amabzala mochedwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Koma tirigu ndi mchewere sizinawonongeke chifukwa zimakhwima mochedwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 9:32
8 Mawu Ofanana  

niwapereka m'manja a Agibiyoni, iwo nawapachika m'phiri pamaso pa Yehova, ndipo anagwa pamodzi onse asanu ndi awiri; m'masiku a kukolola, m'masiku oyamba, poyamba kucheka barele.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Tambasulira dzanja lako padziko la Ejipito, lidze dzombe, kuti likwere padziko la Ejipito, lidye zitsamba zonse za m'dziko, ndizo zonse adazisiya matalala.


Ndipo Mose anatambasulira dzanja lake kuthambo; ndipo munali mdima bii m'dziko lonse la Ejipito masiku atatu;


ndipo lidzakuta nkhope ya dziko, kotero kuti palibe munthu adzakhoza kuona dziko; ndipo lidzadya zotsalira zidapulumuka, zidatsalira inu pamatalala, ndipo lidzadya mtengo uliwonse wokuphukirani kuthengo;


Ndipo thonje ndi barele zinayoyoka; pakuti barele lidafula, ndi thonje lidayamba maluwa.


Ndipo Mose anatuluka kwa Farao m'mzinda nakweza manja ake kwa Yehova; ndipo mabingu ndi matalala analeka, ndi mvula siinavumbanso padziko.


Atakonza thyathyathya pamwamba pake, kodi safesa ponse mawere, ndi kumwazamwaza chitowe, nafesa tirigu m'mizere ndi barele m'malo ake osankhika, ndi mchewere m'maliremo?


Udzitengerenso tirigu, ndi barele, ndi nyemba, ndi mphodza, ndi mapira, ndi mawere, nuziike m'mbale imodzi, ndi kudzipangira mkate nazo; uzidyako monga mwa kuwerenga kwa masiku udzagonawo pambali pako, ndiwo masiku mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa