Eksodo 9:30 - Buku Lopatulika30 Koma inu ndi anyamata anu ndidziwa kuti simudzayamba kuopa nkhope ya Yehova Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma inu ndi anyamata anu ndidziwa kuti simudzayamba kuopa nkhope ya Yehova Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Komabe ndikudziŵa kuti inu ndi nduna zanu simukuwopa Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Koma ine ndikudziwa kuti inu ndi nduna zanu simukuopabe Yehova Mulungu.” Onani mutuwo |