Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 9:30 - Buku Lopatulika

30 Koma inu ndi anyamata anu ndidziwa kuti simudzayamba kuopa nkhope ya Yehova Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Koma inu ndi anyamata anu ndidziwa kuti simudzayamba kuopa nkhope ya Yehova Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Komabe ndikudziŵa kuti inu ndi nduna zanu simukuwopa Chauta.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Koma ine ndikudziwa kuti inu ndi nduna zanu simukuopabe Yehova Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 9:30
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anati, Onani, ndilikutuluka ine kwanu, ndidzapemba Yehova kuti mizaza ichoke mawa kwa Farao, ndi kwa anyamata ake, ndi kwa anthu ake; komatu, Farao asanyengenso ndi kukana kulola anthuwa amuke kukamphera nsembe Yehova.


Mphulupulu iomboledwa ndi chifundo ndi ntheradi; apatuka pa zoipa poopa Yehova.


Ungayanje woipa, koma sadzaphunzira chilungamo; m'dziko la machitidwe oongoka, iye adzangochimwa, sadzaona chifumu cha Yehova.


Yehova bwanji mwatisocheretsa kusiya njira zanu, ndi kuumitsa mitima yathu tisakuopeni? Bwerani, chifukwa cha atumiki anu, mafuko a cholowa chanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa