Eksodo 9:17 - Buku Lopatulika17 Kodi udzikwezanso pa anthu anga, ndi kusawalola amuke? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Kodi udzikwezanso pa anthu anga, ndi kusawalola amuke? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma ukunyozabe anthu anga, osafuna kuŵalola kuti apite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Komabe iwe ukudzitukumula pa anthu anga osawalola kuti atuluke. Onani mutuwo |